Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 15:32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Samueli anati, Bwerani naye kwa ine kuno Agagi mfumu ya Aamaleki. Ndipo Agagi anabwera kwa iye mokondwera. Nati Agagi, Zoonadi kuwawa kwa imfa kunapitirira.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 15

Onani 1 Samueli 15:32 nkhani