Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 14:40 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iye ananena ndi Aisrayeli onse, Inu mukhale mbali yina, ndipo me ndi Jonatani mwana wanga tidzakhala mbali yinanso. Ndipo anthuwo ananena ndi Sauli, Citani cimene cikukomerani.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 14

Onani 1 Samueli 14:40 nkhani