Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 14:28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo wina wa anthuwo anayankha, nati, Atate wanu analangiza anthu kolimba ndi lumbiro, ndi kuti, Wotembereredwa iye wakudya lero cakudya. Ndipo anthuwo analema.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 14

Onani 1 Samueli 14:28 nkhani