Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 14:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo Sauli ananena ndi anthu amene anali naye, Awerenge tsopano, kuti tizindikire anaticokera ndani. Ndipo pamene anawerenga, onani Jonatani ndi wonyamula zida zace panalibe.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 14

Onani 1 Samueli 14:17 nkhani