Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 14:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo a ku kabomawo anayankha Jonatani ndi wonyamula zida zace, nati, Kwerani kuno kwa ife, tikuonetseni kanthu. Ndipo Jonatani anauza wonyamula zida zace, Kwera unditsate m'mbuyo, pakuti Yehova wawapereka m'dzanja la Israyeli.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 14

Onani 1 Samueli 14:12 nkhani