Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 25:16-26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. wacisanu ndi cinai Mataniya, ana ace ndi abale ace khumi ndi awiri:

17. wakhumi Simeyi, ana ace ndi abale ace khumi ndi awiri;

18. wakhumi ndi cimodzi Azareli, ana ace ndi abale ace khumi ndi awiri;

19. wakhumi ndi ciwiri Hasabiya, ana ace ndi abale ace khumi ndi awiri;

20. wakhumi ndi citatu Subaeli, ana ace ndi abale ace khumi ndi awiri;

21. wakhumi ndi cinai Matitiya, ana ace ndi abale ace khumi ndi awiri;

22. wakhumi ndi cisanu Yeremoti, ana ace ndi abale ace khumi ndi awiri;

23. wakhumi ndi cisanu ndi cimodzi Hananiya, ana ace ndi abale ace khumi ndi awiri;

24. wakhumi ndi cisanu ndi ciwiri Yosibekasa, ana ace ndi abale ace khumi ndi awiri;

25. wakhumi ndi cisanu ndi citatu Hanani, ana ace ndi abale ace khumi ndi awiri;

26. wakhumi ndi cisanu ndi cinai Maloti, ana ace ndi abale ace khumi ndi awiri;

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 25