Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 25:14-18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

14. wacisanu ndi ciwiri Yesarela: ana ace ndi abale ace khumi ndi awiri;

15. wacisanu ndi citatu Yesaya, ana ace ndi abale ace khumi ndi awiri;

16. wacisanu ndi cinai Mataniya, ana ace ndi abale ace khumi ndi awiri:

17. wakhumi Simeyi, ana ace ndi abale ace khumi ndi awiri;

18. wakhumi ndi cimodzi Azareli, ana ace ndi abale ace khumi ndi awiri;

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 25