Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 24:7-12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. Ndipo maere oyamba anamgwera Yehoyaribu, waciwiri Yedaya,

8. wacitatu Harimu, wacinai Seorimu,

9. wacisanu Malikiya, wacisanu ndi cimodzi Miyamini,

10. wacisanu ndi ciwiri Hakozi, wacisanu ndi citatu Abiya,

11. wacisanu ndi cinai Yesuwa, wakhumi Sekaniya,

12. wakhumi ndi cimodzi Eliyasibu, wakhumi ndi ciwiri Yakimu,

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 24