Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mbiri 15:28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Momwemo Aisrayeli onse anakwera nalo likasa la cipangano la Yehova ndi kupfuula, ndi kumveka kwa lipenga, ndi mphalasa, ndi nsanje zomveketsa, ndi zisakasa, ndi azeze.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 15

Onani 1 Mbiri 15:28 nkhani