Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 9:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anthu adzayankha, Popeza anasiya Yehova Mulungu wao amene adaturutsa makolo ao m'dziko la Aigupto, natsata milungu yina, nailambira, naitumikira; cifukwa cace Yehova anawagwetsera coipa conseci.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 9

Onani 1 Mafumu 9:9 nkhani