Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 9:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo kunali, atatsiriza Solomo kumanga nyumba ya Yehova, ndi nyumba ya mfumu, ndi cifuniro conse ca Solomo anacikhumbaco,

2. Yehova anaonekera kwa Solomo nthawi yaciwiri, monga momwe adamuonekera ku Gibeoni.

3. Ndipo Yehova anati kwa iye, Ndamva pemphero lako ndi pembedzero lako wandipembedza nalo; ndapatula nyumba imene waimangayi kuikamo dzina langa nthawi zosatha, ndipo maso anga ndi mtima wanga zidzakhala kumeneko masiku onse.

4. Ndipo iwe ukadzayenda pamaso panga, monga momwe Davide atate wako anayendera ndi mtima woona ndi wolungama, kuzicita zonse ndakulamulirazo, ndi kusunga malemba anga ndi maweruzo anga,

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 9