Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 7:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anayenganso thawale lamkuwa, kukamwa kwace kunali kwa mikono khumi, linali lozunguniza, ndi msinkhu wace unali mikono isanu; ndi cingwe ca mikono makumi atatu cinalizungulira.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 7

Onani 1 Mafumu 7:23 nkhani