Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 5:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunacitika, pamene Hiramu anamva mau ace a Solomo, anakondwera kwakukuru, nati, Alemekezeke Yehova lero amene wampatsa Davide mwana wanzeru akhale mfumu ya anthu aunyinji amenewa.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 5

Onani 1 Mafumu 5:7 nkhani