Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 3:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tsopano, Yehova Inu Mulungu wanga, mwalonga ine kapolo wanu ufumu m'malo mwa atate wanga Davide, koma ine ndine kamwana, sindidziwa kuturuka kapena kulowa.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 3

Onani 1 Mafumu 3:7 nkhani