Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 22:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo mfumu ya Israyeli inasonkhanitsa aneneri ngati anthu mazana anai, nanena nao, Kodi ndizimuka kukathira nkhondo pa Ramoti Gileadi, kapena ndileke? Nati iwo, Kweraniko; popeza Ambuye adzaupereka m'dzanja la mfumu.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 22

Onani 1 Mafumu 22:6 nkhani