Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 20:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anati kwa mithenga ya Benihadadi, Kauzeni mbuye wanga mfumu, Zonse munayamba kundituma mtumiki wanu kuzifunsa ndidzacita, koma ici sindingacicite. Nicoka mithengayo, nimbwezera mau.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 20

Onani 1 Mafumu 20:9 nkhani