Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 20:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

koma mawa dzuwa lino ndidzatuma anyamata anga kwa iwe, nadzafunafuna m'nyumba mwako, ndi m'nyumba za anyamata ako; ndipo kudzakhala kuti cifuniro conse ca maso ako adzacigwira ndi manja ao, nadzacicotsa.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 20

Onani 1 Mafumu 20:6 nkhani