Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 20:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anyamata a mfumu ya Aramu anati kwa iye, Milungu yao nja kumapiri, ndimo m'mene atilakira; koma tikaponyana nao kucidikha, zedi tidzaposa mphamvu.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 20

Onani 1 Mafumu 20:23 nkhani