Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 2:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ucitire zokoma ana amuna aja a Barizilai wa ku Gileadi, akhale pakati pa akudyera pa gome lako, popeza momwemo amenewo anandiyandikira muja ndinalikuthawa Abisalomu mbale wako.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 2

Onani 1 Mafumu 2:7 nkhani