Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 2:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Pakuyandikira masiku ace a Davide akuti amwalire, analamulira Solomo mwana wace, nati,

2. Ndimuka ine njira ya dziko lonse: limba mtima tsono, nudzionetse umunthu;

3. nusunge cilangizo ca Yehova Mulungu wako, kuyenda m'njira zace, kusunga malemba ndi malamulo ndi maweruzo ndi umboni wace, monga mulembedwa m'cilamulo ca Mose, kuti ukacite mwa nzeru m'zonse ukacitazo, ndi kumene konse ukatembenukirako;

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 2