Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 19:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo atamva Eliya, anapfunda nkhope yace ndi copfunda cace, naturuka, naima pa khomo la phangalo. Ndipo taonani, anamdzera mau akunena naye, Ucitanji kuno, Eliya?

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 19

Onani 1 Mafumu 19:13 nkhani