Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 19:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iye anati, Turuka, nuime pa phiri tino pamaso pa Yehova. Ndipo taonani, Yehova anapitapo, ndi mphepo yaikuru ndi yamphamvu inang'amba mapiri, niphwanya matanthwe pamaso pa Yehova; koma Yehova sanakhala m'mphepomo. Itapita mphepoyo kunali cibvomezi; komanso Yehova sanali m'cibvomezico.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 19

Onani 1 Mafumu 19:11 nkhani