Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 17:22-24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

22. Ndipo Yehova anamvamau a Eliya, ndipo moyo wa mwanayo unalowanso mwa iye, nakhalanso moyo.

23. Ndipo Eliya ananyamula mwanayo, natsika naye ku cipinda cosanja, nalowa naye m'nyumba, nampereka kwa amace; nati Eliya, Taona, mwana wako ali moyo.

24. Ndipo mkazi anati kwa Eliya, Ndizindikira tsopano kuti ndinu munthu wa Mulungu, ndi kuti mau a Yehova ali m'kamwa mwanuwo ngoona.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 17