Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 16:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma anthu aja omangira misasa anamva kuti Zimri wacita ciwembu, nakanthanso mfumu; cifukwa cace tsiku lomwelo Aisrayeli onse a kumisasa anamlonga Omri kazembe wa nkhondo akhale mfumu ya Israyeli.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 16

Onani 1 Mafumu 16:16 nkhani