Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 16:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo caka ca makumi awiri mphambu zisanu ndi ziwiri ca Asa mfumu ya Yuda, Zimri anali mfumu masiku asanu ndi awiri ku Tiriza. Ndipo anthu analikumangira misasa Gibetoni wa Afilisti.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 16

Onani 1 Mafumu 16:15 nkhani