Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 15:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo macitidwe onse ena a Asa, ndi mphamvu yace yonse, ndi zonse anazicita, ndi midzi anaimanga, kodi sizilembedwa m'buku la macitidwe a mafumu a Yuda? Koma masiku a ukalamba wace anadwala mapazi ace.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 15

Onani 1 Mafumu 15:23 nkhani