Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 14:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunacitika, pamene Ahiya anamva mgugu wa mapazi ace alinkulowa pakhomo, anati, Lowa mkazi iwe wa Yerobiamu, wadzizimbaitsiranji? pakuti ine ndatumidwa kwa iwe ndi mau olasa.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 14

Onani 1 Mafumu 14:6 nkhani