Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 13:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunacitika, pa kumva mfumu mau a munthu wa Mulungu amene anawapfuula, kutemberera guwa la nsembe m'Beteli, Yerobiamu anatansa dzanja lace ali ku guwalo, nati, Mgwireni iye. Ndipo dzanja lace analitansira kwa iye linauma, kuti sanatha kulipfunyatitsanso.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 13

Onani 1 Mafumu 13:4 nkhani