Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 12:33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anapereka nsembe pa guwa la nsembe analimanga m'Beteli, tsiku lakhumi ndi cisanu la mwezi wacisanu ndi citatu, m'mwezi umene anaulingirira m'mtima mwa iye yekha, nawaikira ana a Israyeli madyerero, napereka nsembe pa guwa la nsembe, nafukiza zonunkhira.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 12

Onani 1 Mafumu 12:33 nkhani