Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 12:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pakuona Aisrayeli onse kuti mfumu siinawamvera iwo, anthuwo anayankha mfumu, Tiri naye ciani Davide? inde tiribe colowa m'mwana wa Jese; tiyeni kwathu Aisrayeli inu; yang'aniranitu, nyumba yako, Davide. Momwemo Aisrayeli anacoka kumka ku mahema ao.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 12

Onani 1 Mafumu 12:16 nkhani