Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 12:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo acinyamata anzace ananena naye, Dati, Mzitero ndi anthu awa adalankhula nanu, nati, Atate wanu analemeretsa gori lathu, koma inu mutipepuzire limenelo; mzitero nao, Kanense wanga adzaposa m'cuuno mwa atate wanga.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 12

Onani 1 Mafumu 12:10 nkhani