Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 11:38 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kudzakhala kuti ukadzamvera iwe zonse ndikulamulirazo, nukadzayenda m'njira zanga ndi kucita cilungamo pamaso panga, kusunga malemba anga ndi malamulo anga, monga anatero Davide mtumiki wanga pamenepo Ine ndidzakhala ndi iwe, ndidzakumangira ndi kukukhazikitsira nyumba, monga nelinammangira Davide, ndipo ndidzakupatsa iwe Israyeli.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 11

Onani 1 Mafumu 11:38 nkhani