Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 11:31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nati kwa Yerobiamu, Takwaya magawo khumi; popeza atero Yehova Mulungu wa Israyeli, Taona ndidzaung'amba ufumu m'dzanja la Solomo ndi kukupatsa iwe mafuko khumi.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 11

Onani 1 Mafumu 11:31 nkhani