Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 11:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsono Farao anati kwa iye, Koma cikusowa iwe nciani kwa ine, kuti ufuna kumuka ku dziko la kwanu? Nayankha iye, Palibe kanthu, koma mundilole ndimuke ndithu.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 11

Onani 1 Mafumu 11:22 nkhani