Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 10:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Wolemekezeka Yehova Mulungu wanu amene anakondwera nanu, kukuikani pa mpando wacifumu wa Israyeli; popeza Yehova anakonda Israyeli nthawi yosatha, cifukwa cace anakulongani inu ufumu, kuti mucite ciweruzo ndi cilungamo.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 10

Onani 1 Mafumu 10:9 nkhani