Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 10:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mkaziyo ananinkha mfumu matalenti a golidi zana limodzi mphambu makumi awiri, ndi zonunkhira zaunyinji, ndi timiyala ta mtengo wapatali; sunafikanso unyinji wotero wa zonunkhira wolingana ndi uja mfumu yaikazi inapereka kwa mfumu Solomo.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 10

Onani 1 Mafumu 10:10 nkhani