Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 1:39 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Zadoki wansembe anatenga nyanga ya mafuta inali m'Cihema, namdzoza Solomo. Ndipo iwo anaomba lipenga, ndi anthu onse anati, Mfumu Solomo akhale ndi moyo.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 1

Onani 1 Mafumu 1:39 nkhani