Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 1:38 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo Zadoki wansembe, ndi Natani mneneri, ndi Benaya mwana wa Yehoyada, ndi Akereti, ndi Apeleti aja anatsika, nakweza Solomo pa nyuru ya mfumu Davide, nafika naye ku Gihoni.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 1

Onani 1 Mafumu 1:38 nkhani