Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 1:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tsopano, mbuye wanga mfumu, maso a Aisrayeli onse ali pa inu, kuti muwauze amene adzakhala pa mpando wacifumu wa mbuye wanga mfumu atamuka iye,

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 1

Onani 1 Mafumu 1:20 nkhani