23. Wa ana a Yosefe; wa pfuko la ana a Manase, kalonga Haniyeli mwana wa Efodi.
24. Wa pfuko la ana a Efraimu, kalonga Kemuyeli mwana wa Sipitana.
25. Wa pfuko la ana a Zebuloni, kalonga Elisafana mwana wa Paranaki.
26. Wa pfuko la ana a Isakara, kalonga Palitiyeli mwana wa Azana.