1. MAU a Mlaliki, mwana wa Davide, mfumu ya m'Yerusalemu.
2. Zacabecabe, ati Mlaliki; zacabecabe zonse ndi cabe.
3. Kodi nchito zace zonse munthu asauka nazo zimpindulira ciani?
4. Mbadwo wina opita, mbadwo wina nufika; koma dziko lingokhalabe masiku onse,