1. Muyeso wonyenga unyansa Yehova;Koma mulingo wamphumphu umsekeretsa.
2. Pakudza kudzikuza padzanso manyazi;Koma nzeru iri ndi odzicepetsa,
3. Kuongoka mtima kwa olungama kuwatsogolera;Koma kukhota kwa aciwembu kudzawaononga.
4. Cuma sicithandiza tsiku la mkwiyo;Koma cilungamo cipulumutsa kuimfa.