19. Koma adani anga ali ndi moyo, nakhalandi mphamvu:Ndipo akundida kopanda cifukwa acuruka.
20. Ndipo iwo akubwezera coipa pa cabwinoAtsutsana nane, popeza nditsata cabwino.
21. Musanditaye, Yehova:Mulungu wanga, musakhale kutali ndi ine.
22. Fulumirani kundithandiza,Ambuye, cipulumutso canga.