3. Ngati ndidzalowa pakhomo pa nyumba yanga,Ngati ndidzakwera pa kama logonapo;
4. Ngati ndidzalola maso anga agone,Kapena zikope zanga ziodzere;
5. Kufikira nditapezera Yehova malo,Cokhalamo Wamphamvuyo wa Yakobo?
6. Taonani, tinacimva m'Efrata;Tinacipeza ku cidikha ca kunkhalango.