Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yuda 1:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Mikayeli mkulu wa angelo, pakucita makani ndi mdierekezi anatsutsana za thupi la Mose, sanalimbika mtima kumehulira cifukwa comcitira mwano, koma anati, Ambuye akudzudzule.

Werengani mutu wathunthu Yuda 1

Onani Yuda 1:9 nkhani