Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 8:45-49 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

45. Koma Ine, cifukwa ndinena coonadi, simukhulupirira Ine.

46. Ndani mwa inu anditsutsa Ine za cimo? Ngati ndinena coonadi, simundikhulupirira Ine cifukwa ninji?

47. 6 Iye wocokera kwa Mulungu amva zonena za Mulungu; inu simumva cifukwa cakuti simuli a kwa Mulungu,

48. Ayuda anayankha nati kwa iye, Kodi sitinenetsa kun Inu ndinu Msamariya, ndipo 7 muli ndi ciwanda?

49. Yesu anayankha, Ndiribe ciwanda Ine; koma ndilemekeza Atate wanga, ndipo inu mundipeputsa.

Werengani mutu wathunthu Yohane 8