Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 8:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Anayankha Yesu nati kwa iwo, Ndingakhale ndicita umboni wa Ine ndekha umboni wanga uli woona; cifukwa ndidziwa kumene ndinacokera ndi kumene ndimukako; koma e inu, simudziwa kumene ndicokera, ndi kumene ndimukako.

Werengani mutu wathunthu Yohane 8

Onani Yohane 8:14 nkhani