Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 8:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Koma Yesu anamuka ku phiri la Azitona.

2. Komac mamawa anadzanso kuKacisi, ndipo anthu onse anadza kwa iye; ndipo m'mene anakhala pansi anawaphunzitsa.

3. Koma alembi ndi Afarisi anabwera naye kwa iye mkazi wogwidwa m'cigololo, ndipo pamene anamuimika iye pakati,

4. ananena kwa iye, Mphunzitsi, mkazi uyu wagwidwa alimkucita cigololo.

Werengani mutu wathunthu Yohane 8