Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 6:62-67 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

62. 15 Nanga bwanji ngati mukaona Mwana wa munthu alikukwera kumene anali kale lomwe?

63. 16 Wopatsa moyo ndi mzimu; thupi silithandiza konse. Mau amene ndalankhula ndi inu ndiwo mzimu, ndi moyo.

64. Koma 17 pali ena mwa inu amene sakhuluplra, Pakuti. Yesu anadziwa poyamba amene ali osakhulupira, ndi amene adzampereka.

65. Ndipo ananena, 18 Cifukwa ca ici ndinati kwa inu, kuti palibe munthu angathe kudza kwa Ine, koma ngati kupatsidwa kwa Iye ndi Atate.

66. 19 Pa ici ambiri a akuphunzira ace anabwerera m'mbuyo, ndipo sanayenda-yendanso ndi iye.

67. Cifukwa cace Yesu anati kwa khumi ndi awiriwo, Nanga inunso mufuna kucoka?

Werengani mutu wathunthu Yohane 6