Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 6:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Gwirani nchito si cifukwa ca cakudya cimene citayika koma ca cakudya cimene citsalira ku moyo wosatha, cimene Mwana wa munthu adzakupatsani inu; pakuti ameneyo Atate, ndiye Mulungu, adamlembera cizindikilo.

Werengani mutu wathunthu Yohane 6

Onani Yohane 6:27 nkhani